Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

158. Masika A Dziko Ayandika

HASTEN ON, GLAD DAY

HASTEN ON, GLAD DAY

1. Masika a dziko ayandikatu,
Aitana Mbuye okololawo;
Ndi minda yayera pa dziko lonse,
Ndi mwini zotuta wayandikanso.

*CHORUS:
’Dzanitu msanga, Tengatu zotuta;
Mdzatitenge ’fe, Kwathuko.
*

*(Alto, Tenor, and Bass):
Idzanitu angelo, msangatu;
Tengerani zotuta mmwambamo.
Mudzatengetu ife, kunkatu,
Kwathu mmwambamo.
*

2. E, tsiku lopanda misozi konse,
Layandika kudza mothamangatu;
Akubalalika ndi uchimowo,
Mwasonkhetu nthawi isanathei.

3. Ikomatu ntchito ya chikondicho,
Kasupe wosaphwa wa kumwambako;
Chikonditu ndicho chiitana ’fe,
Chigwiritsa ntchito, chibalitsatu.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 158

Permanent page: number and title URL

This page preserves Masika A Dziko Ayandika as Hymn 158 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.