Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

178. Mmamawa Kapena Potuluka Dzuwa

CHRIST RETURNETH

CHRIST RETURNETH

1. Mmamawa kapena potuluka dzuwa,
Ambuye Yesuyo ’dzafika ndi mphamvu,
Ndi ulemerero wo’kulu kutenga
Anthu ake mu dzikoli.

*CHORUS:
Yesu, Mbuye wathu,
’Dzayimba mokondwa liti?
Khristu adza, Khristu adza,
Aleluya amen. Aleluya amen.*

2. Kapena usana kapena madzulo,
Kapena usiku pamene Ambuye
’Dzafika mu ulemelero kutenga
Anthu ake mu dzikoli.

3. Tidzakondwa ngati tidzanka osafa,
Opanda kudwala, chisoni, maliro;
Kungokhwathulidwa podzadza kutenga
Anthu ake mu dzikoli.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 178

Permanent page: number and title URL

This page preserves Mmamawa Kapena Potuluka Dzuwa as Hymn 178 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.