Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
190. Konda Dzina La Yesu
PRECIOUS NAME
PRECIOUS NAME
1. Konda dzinalo la Yesu,
Mwana wosauka ’we,
Ndilo lothandiza anthu,
Khala nalo ponse phee.
*CHORUS:
Dzina la Yesuyo,
Lokondwetsa onsewo.
Mwambamo, ponsepo,
Litonthoza m’mtimamo.*
2. Konda dzinalo la Yesu,
M’moyo mwanu monsemo;
Mmene muli kuyesedwa,
Tchula dzina lakelo.
3. Dzina ili ndi lokoma,
La Mombolo wathuyo,
Polandira ife mmwamba
Tidzakondwererako.
4. Mbuye Yesu timtamanda,
Ndi zinyimbo zathuzo;
Mfumu ya mafumu onse,
Yesu timayesadi.
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 190
Permanent page: number and title URL
This page preserves Konda Dzina La Yesu as Hymn 190 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.