Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
193. Kodi Ungakhale Moyo Wonga Wacewo?
HIS WAY WITH THEE
HIS WAY WITH THEE
1. Kodi ungakhale moyo wonga Wakewo?
Kumayenda naye m’njira monsemo?
Ungamlole Iye kunyamula nkhawazo?
Mlole atsogole ’Ye.
*CHORUS:
Mwa mphamvu Yake udzakhalatu,
Wakumasuka, inde, m’mwazi ’ke.
Chikondi ’ke chidzaze mtimako,
Poyenda nawe zidamkonda ’Ye.*
2. Ungamlole kuti Iye amasule ’we?
Kuti umutsate poitana ’Ye?
Ungamlole kukutchinjiriza Mbuyeyo?
Mlole atsogole ’Ye.
3. Monga ukapeza malo mu ufumuwo?
Ungamyese akusamalire ’we?
Ungagwire ntchito Yake kopambanadi?
Mlole atsogole ’Ye.
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 193
Permanent page: number and title URL
This page preserves Kodi Ungakhale Moyo Wonga Wacewo? as Hymn 193 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.