Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
195. Tifuna Mzimu wanuyo
O FOR THAT FLAME!
O FOR THAT FLAME!
1. Tifuna Mzimu wanuyo,
Yemwe nawala kalelo;
Nawatenthetsa m’mtimamo,
Nawalimbitsa mzo’psamo.
2. Mzimuyo ali kuti ko,
Nadzazayo Abramuyo?
Namsintha mtima Paulo,
Yemwe nampatsa changucho?
3. Yemwenso kalekalelo
Nanena za chikondicho,
Nawala pa Yesayayo,
Nampatsa Daniel nzeruzo.
4. Kodi mulibe mphamvuzo
Monga Eliya nazimva?
Mose nawala nkhopeyo,
Yobu anapiriranso?
5. M’chitetu monga kalelo,
Dzutsani ntchito yanuyo.
M’mene tipempha kwanuko,
Mtitsanulire Mzimuyo.
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 195
Permanent page: number and title URL
This page preserves Tifuna Mzimu wanuyo as Hymn 195 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.