Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
214. Kodi Yesu Asamala
DOES JESUS CARE?
DOES JESUS CARE?
1. Kodi Yesu asamalira
Nkasowa cimwemwe;
Ndikapsinjika ndi kuda nkhawa
M’njira yonse yaitari?
* CHORUS:
Ndidziwa amasamala, Inde ndikabvutika;
Ndithu masana ndi usiku amandisamalirane.
*
2. Kodi yesu asamalitsa
Mu’siku woopsa,
Pamene kwada zoopsa zadza,
Andisamalabe kodi?
3. Kodi Yesu asamalitsa
Ndikagwa m’mayeso?
Mwa za cisoni zosapumitsa,
Misozi usiku wonse?
4. Kodi Yesu asamalitsa
Poleka za dziko,
Ndiri kuthatha pafupi kufa
Kodi akundionadi?
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 214
Permanent page: number and title URL
This page preserves Kodi Yesu Asamala as Hymn 214 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.