Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

225. Uyang’ane Mdaniyo

STAND LIKE THE BRAVE

STAND LIKE THE BRAVE

1. Mkhristuwe dzuka! Alamula Mbuye;
Tenga cikopa, ndi lupanga m’dzanja,
Ukomane naye, usamuope
Ulimbe Mtima, Myang’ane mdaniyo.

* Refrain:
Limba Mtima, Limba Mtima,
Limba Mtima, Pom’yang’ana mdani.
*
2. Zoopsa ziripo, ucenjeretu,
Usafulatire, ungapwekekwe;
Unyinji wa ’dani, udzagonjetsa,
Ulimbe Mtima, M’yang’ane mdaniyo.

3. Ntchito ya Mbuyako uiteteze;
Dzukatu mwa cangu nkhondoyo ithe;
Akakulamula, pita mwa cangu,
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo.

4. Pita limbikira, suli wekhai,
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Mwayi apatsa, cisangalatsonso;
Cikondi cace ngati mtsinje m’tengo;
Ulimbe Mtima M’yang’ane mdaniyo

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 225

Permanent page: number and title URL

This page preserves Uyang’ane Mdaniyo as Hymn 225 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.