Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

255. Ndikusowani Yesu

I NEED THEE PRECIOUS JESUS

I NEED THEE PRECIOUS JESUS

1. Ndikusowani Yesu, Ndiri waumphawi;
Mlendo wopanda malo, Za dziko ndilibe.
A Yesu Mudnikonde, Mundicingamire,
Ndikunditsogolera, Mphamvu yanga ndinu.

2. Ndisowa Mtima wanu, Kudziwa nkhawazo,
Ndi mayesero anga, Ndi zacisonizo.
Nsowa Mzimu Woyera, Womandiphunzitsa,
Kundiuzane Yesu, Ndi Mwana wa nkhosa.

3. Ndikusowani Yesu, Ndionane nanu,
Mu uta-wa-lezamo, Pa cimpando canu.
Ndi ogulidwa m’mazi, Ndikakondwerere
Nyimbo zosadukiza, Ndikumpenyetsetsa.

Amen.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 255

Permanent page: number and title URL

This page preserves Ndikusowani Yesu as Hymn 255 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.