Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

284. Popita Masikuwa

WHILE THE DAYS ARE GOING BY

WHILE THE DAYS ARE GOING BY

1. Kuli anthu obvutika, Popita masikuwa,
Kuli anthu akutopa, Popita masikuwa;
Ngati tiwakondwetsa, Poyenda ulendowu
Zabwino ticitetu, Popita masikuwa.

* CHORUS:
Masiku apita, Masiku apita,
Zabwino ticitetu! Popita masikuwa.
*
2. Kulibe nthawi yotaya, Popita masikuwa;
Mukhale osangalala, Popita masikuwa;
Dziko liri m’cisoni, Misozi ndi maliro;
Thandiza obvutika, Popita masikuwa.

3. Zotimanga tizisiya, Popita masikuwa;
Modzi ndi mmodzi atsala, Popita masikuwa
Zabwino tidzakhala, ponse ponse zimera;
Tidzakhala okondwa, Popita masikuwa.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 284

Permanent page: number and title URL

This page preserves Popita Masikuwa as Hymn 284 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.