Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

299. Tikondwere Nthawi Zonse

ALWAYS CHEERFUL

ALWAYS CHEERFUL

1. Tikondwere nthawi zonse; Tidandauliranji
Kwina "Tate wathu Mlungu, Atisamalirafe?

* CHORUS:
Tikondwere nthawi zonse Ponse dzuwa liwala
Njira ya ntchitoyi ndi yokoma
Tikondwere konseko.
*
2. Dzanja lace litsogoza, Ngati chimo lidzatu
Nsisi zace, Satisiya tokha bi.

3. Tikaleka ntchito yathu, Tidzacita macimo,
Ndipo mtambo wa cisoni, Udzaletsa cimwemwe.

4. Abwinowo akondwere, Ndi mtendere wosatha
Timveretu mau ace, Tikonde zokomazo.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 299

Permanent page: number and title URL

This page preserves Tikondwere Nthawi Zonse as Hymn 299 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.