Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

58. Mumbveke Mbuyeyo

ALL HAIL THE POWER

ALL HAIL THE POWER

1. Tamani mphamvu ya Yesu angelo agwade;
Tulutsanitu korona mumveke Mbuyeyo
Tulutsanitu korona mumveko Mbuyeyo.

2. Inu osankhidwa ake, Owomboledwa’nu,
Tamani Mpulumutsiyo, mumveke Mbuyeyo;
Tamani Mpulumutsiyo mumveko Mbuyeyo.

3. Anthu onse ndi mitundu, Pa dziko linotu,
Am’lemekeze Mfumuyo, mumveke Mbuyeyo;
Am’lemekeze Mfumuyo, mumveke Mbuyeyo.

4. Tifuna kuti komweko, Tikamgwadire’Ye
Tidzayimba kosaleka mumveke Mbuyeyo
Tidzayimba kosaleka mumveke Mbuyeyo.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 58

Permanent page: number and title URL

This page preserves Mumbveke Mbuyeyo as Hymn 58 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.