Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

233. Uzeni Nthano Yakale

TELL ME THE OLD, OLD STORY

TELL ME THE OLD, OLD STORY

1. Uze nthano yakale, Ya za kumwambako,
Za Yesu wacifundo, Za Yesu wokonda;
Pang’ono pang’onotu, monga kwa kamwana,
Poti ndiri wotopa, wopanda thandizo.

* CHORUS:
Nthano yakale uze, Nthano yakale uze,
Nthano yakale uze, Ya Yesu wokonda.
*
2. Pang’ono ndi pang’ono, Motsimikizadi;
Pakuti ndaipadi, Yesu nandifera;
Nthano yonseyo uze, Musacite mphwayi,
M’nthawi yonse ya bvuto, Andisangalatsa.

3. Nenatu yomwe ija, Ukhala ndi mantha,
Kuti dziko loipa, Ndilikondetsetsa;
Ulemu wa dzikowu Uyamba m’moyomu,
Uze nthano yakale; Yesu akuciza.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 233

Permanent page: number and title URL

This page preserves Uzeni Nthano Yakale as Hymn 233 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.