Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
274. Ndiri Ndi Mbuye
I HAVE A SAVIOUR
I HAVE A SAVIOUR
1. Ndiri ndi Mbuye wodandaulira,
Akonda Iyeyu kuposa dziko;
Pano andiyang’anira mwacifundo,
Ndifunatu akhale wa inunso!
* CHORUS:
Ndipempherera’nu, Ndipempherera’nu,
Ndipempherera’nu, Ndipempherera’nu,
*
2. Ndiri ndi Tate andipatsa ine
Ciyembekezo ca moyo wosatha;
Sacedwa kuitana tipite kwathu;
Ndifuna adzalandire inunso!
3. Ndiri n’zobvala, zopanda mabanga
Aindilindira mu ulemelero;
Wowalal monsemo konko ndizalandira,
Bwenzi ndifuna ukalandirenso!
4. Pamene Yesu wakupeza iwe,
Tauzatu ena za mtendererewo
Mwini ndiye Kristu yemweyo apatsa,
Mtendere ndifuna mulandirenso!
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 274
Permanent page: number and title URL
This page preserves Ndiri Ndi Mbuye as Hymn 274 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.