Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

275. Kosatha! N’kuti?

ETERNITY - WHERE

ETERNITY - WHERE

1. "Kosatha! - n’kuyi?" Ndilo funsolo;
Konse komwe uli liri komweko!
Udzakhala kuti nthawi zosatha!
Udzakhala kuti nthawi zosatha!

2. "Kosatha! N’kuti?" Kosatha n’kuti?
Ndi oomboledwa? Ndi otaika?
Mbali izi njiti - "Kosatha! N’kuti?"
Mbali izi njiti - "Kosatha! N’kuti?"

3. "Kosatha! N’kuti?" Uchitiranji
Zokondwa za dziko mosaganiza?
Popanda kusankha - "Kosatha! N’kuti?"
Popanda kusankha - "Kosatha n’kuti?

4. "Kosatha! N’kuti?" Bwenzi samala;
Adzaweruzatu Mulungu msanga
Lero linganene - "kosatha! N’kuti?"
Lero linganene - "Kosatha! N’kuti?

5. "Kosatha! N’kuti?" Kosatha! N’kuti?"
Bwenzi usagone, lekana m’dziko,
Mpaka utayankha - "Kosatha! N’kuti?"
Mpaka utayankha - "Kosatha! N ’kuti.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 275

Permanent page: number and title URL

This page preserves Kosatha! N’kuti? as Hymn 275 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.