Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
282. Mingoli Zikwi Khumi
TEN THOUSAND HARPS
TEN THOUSAND HARPS
1. Ha! Mingoli ndi maunso Alemekeza m’mwamba;
Yesu m’mwambamo akondwa; Alamula ponsepo;
Ali pa mpando uko; Yesu alamulira
Aliluya! Aliluya! Aliluya! Amen
2. Krona wanu sabvulidwa, Mfumu yolemerera;
Cikondi canu cosatha, Kwa anthu onse;
Anthu anu okondwa Adzaona nkhopeyo
Aliluya! Aliluya! Aliluya! Amen.
3. Ambuye idzani msanga tsikulo tilisowa
Kudzamvetsera tsikulo, m’mwamba ndi dziko zatha’
Tidzaliza mingoli Ulemu kwa Mfumuyo.
Aliluya! Aliluya! Aliluya! Amen.
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 282
Permanent page: number and title URL
This page preserves Mingoli Zikwi Khumi as Hymn 282 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.