Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
30. Dzuwa Lili Kulowa
DAY IS DYING IN THE WEST
DAY IS DYING IN THE WEST
1. Dzuwa lili kulowa, Mlungu atipumitse;
Linda ndi kupemphera mmene nyali zili kuwala m’mwamba.
*CHORUS:
Woyera Ambuye wa makamu!
Za m’mwamba ndi za dziko zitamanda Inu,
Mlungu Wamkulu.
*
2. Ambuye wamoyo’Nu, Ife tasonkhanatu,
Kufuna nkhope Yanu; mutifungatire’fe m’khola Lanu
3. Pamene mthunzi ugwa, Mumatifungatira;
Mwa chisomo chanutu, Mitima yathu ikwera kwa Inu.
4. Tikamwalira ife osaona za dziko,
Ambuye wachifundo, mutidzutsenso tsiku lotsiriza.
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 30
Permanent page: number and title URL
This page preserves Dzuwa Lili Kulowa as Hymn 30 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.