Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

30. Dzuwa Lili Kulowa

DAY IS DYING IN THE WEST

DAY IS DYING IN THE WEST

1. Dzuwa lili kulowa, Mlungu atipumitse;
Linda ndi kupemphera mmene nyali zili kuwala m’mwamba.

*CHORUS:
Woyera Ambuye wa makamu!
Za m’mwamba ndi za dziko zitamanda Inu,
Mlungu Wamkulu.
*
2. Ambuye wamoyo’Nu, Ife tasonkhanatu,
Kufuna nkhope Yanu; mutifungatire’fe m’khola Lanu

3. Pamene mthunzi ugwa, Mumatifungatira;
Mwa chisomo chanutu, Mitima yathu ikwera kwa Inu.

4. Tikamwalira ife osaona za dziko,
Ambuye wachifundo, mutidzutsenso tsiku lotsiriza.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 30

Permanent page: number and title URL

This page preserves Dzuwa Lili Kulowa as Hymn 30 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.