Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

29. Mukhale Ndine

ABIDE WITH ME

ABIDE WITH ME

1. Mukhale ndine dzuwa lalowa, Wagwa usiku bwenzi lisowa,
Ndilibe wina wondithandiza, Wa mphamvu ndinu, mkhale ndinetu.

2. Kamoyo kanga katha leroli, Zidzachokanso zinthu za dziko,
Zimasinthika zoonekazo, Simusinthika mkhale ndinetu.

3. Koma kale mnakhalitsa pano, Mukhale ndine musachokenso,
Simpempha kuti Mbuye mutsotse, Komatu mukhalitse ndinetu.

4. Ndifuna inu tsiku lonselo, Ndi mphamvu yanu ndidzasungika,
Mukatsogola sindiopai, Msana, usiku, mkhale ndinetu.

5. Adani sindiopa mulipo, Muletse tsoka ndi chisonichi,
Ikadza imfa ndzalimba mtima, M’imfa ndi moyo mkhale ndinetu.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 29

Permanent page: number and title URL

This page preserves Mukhale Ndine as Hymn 29 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.