Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
78. Kupulumutsa Omwe Ali Kufa
RESCUE THE PERISHING
RESCUE THE PERISHING
1. Pulumutsa omwe ali kufatu,
Uwachotse m’manda a uchimo;
Lilira ochimwa, nuwadzutsetu,
Nuwauze za Yesu Mbuyeyo.*
*
*CHORUS:
Pulumutsa omwe ali kufatu,
Yesu wachifundo alanditsa.*
2. Ngakhale amkana, Iye alinda,
Afuna kulandira olapa.
Awapembedzera moona Mtima,
Adzawakhululukira iwo.
3. Mu Mtima wa munthu muli zambiri,
Koma Yesu azichotsa zonse;
Atakhudzidwa ndi chikondi chake,
Nsinga za Satana zidzaduka.
4. Pulumutsa omwe ali kufatu
Limbitsa othodwa ndi olema;
Kwabwezera m’njira yopapatiza,
Ndi kuwauza za Mpulumutsi
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 78
Permanent page: number and title URL
This page preserves Kupulumutsa Omwe Ali Kufa as Hymn 78 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.