Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa
77. Kufunafuna Otaikawo
SEEKING THE LOST
SEEKING THE LOST
1. Kufunatu E! ndi mtina wonse,
Kufuna akusocherawo;
Lalika kuti Yesu anati,
Idzani nonse kwa Inetu.*
*
*CHORUS:
Pitanitu (inde) konse konseko,
Mukabwere ndi (anthu) osochera;
M’khola lake la (Yesu) Mpulumutsi.
Nafera’Ye anthu (E) ochimwa.*
2. Kufunatu ndi kutsogolera,
Anthu ofoka’wo kwa Yesu;
Kutsogolera njira yabwino,
Yonka ku moyotu wosatha.
3. Tidzitero ponka kulalika,
Kutsata Yesu tsiku n’tsiku;
Ndi kuthangata ofoka onse,
Kuwatsogolera kwa Yesu.
Help keep these hymns free
Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.
♥ DonateHymn details
Hymnal: Khristu Mu Nyimbo
Search name: Christ in Song Chichewa
Language: Chichewa
Hymn number: 77
Permanent page: number and title URL
This page preserves Kufunafuna Otaikawo as Hymn 77 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.
Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.
Reading and preservation note
Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.