Christ in Song Christ in Song Chichewa

Khristu Mu Nyimbo · Christ in Song Chichewa

38. Limbikani Mwa Mulungu

FIRMLY STAND FOR GOD

FIRMLY STAND FOR GOD

1 Limbikani mwa Mlungu wanuyo,
Nkana m’dziko muli mavutowo;
Khristu ndiye thanthwe lolimbalo,
Ndi la mphamvu zonsezo.

*CHORUS:
Tilimbike kuima pa thanthwe lija,
Thanthwe ndilo Khristuyo;
Ngati tipiriratu tidzankako,
Kuli mpando wa Mlunguyo.
*
2 Limbikani ndi mtima woti nji,
Inde mwa chikhulupirirocho;
Kristu ndiye thanthwe la mphamvulo,
Agonjetsa tchimolo.

3 Limbikani mwa choonadicho,
Chikuthangatani koposatu;
Kristu ndiye thanthwe lopumamo,
Mmene vuto latha phe.

Help keep these hymns free

Your donation can help maintain the website, improve accessibility and keep the hymns freely available.

Hymn details

Hymnal: Khristu Mu Nyimbo

Search name: Christ in Song Chichewa

Language: Chichewa

Hymn number: 38

Permanent page: number and title URL

This page preserves Limbikani Mwa Mulungu as Hymn 38 in Khristu Mu Nyimbo. It is part of the Christ in Song Chichewa collection within a multilingual Adventist hymn archive built for reading, searching, sharing and comparing hymn traditions across languages.

Use the previous and next buttons to continue through this hymnal, or return to the collection page to search by number and title. The reading tools above let you adjust text size, save favourites and share the hymn with others.

Reading and preservation note

Historic and regional hymn texts can contain spelling differences, older punctuation, local wording and transcription variations. This archive keeps the hymns searchable while allowing future corrections and improvements to be made carefully.